Ezekieli 40:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

M'masomphenya a Mulungu Iye anabwera nane m'dziko la Israyeli, nandikhalitsa pa phiri lalitali ndithu; pamenepo panali ngati mamangidwe a mudzi kumwela,

Ezekieli 40

Ezekieli 40:1-9