Yesaya 66:21-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. Ndipo ena a iwo ndidzawatenga akhale ansembe ndi Alevi, ati Yehova.

22. Pakuti monga m'mwamba mwatsopano ndi dziko lapansi latsopano limene ndidzalenga, lidzakhalabe pamaso pa Ine, ati Yehova, momwemo adzakhalabe ana anu ndi dzina lanu.

23. Ndipo kudzakhala kuti kuyambira pa mwezi wokhala kufikira ku unzace, ndi kuyambira pa Sabata lina kufikira ku linzace, anthu onse adzafika kudzapembedzera pamaso pa Ine, ati Yehova.

Yesaya 66