Yesaya 37:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace, Yehova, Mulungu wathu, mutipulumutse ife m'manja mwace, kuti maufumu onse a dziko adziwe, kuti Inu ndinu Yehova, Inu nokha.

Yesaya 37

Yesaya 37:16-24