Yeremiya 2:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

amene ati kwa mtengo, Iwe ndiwe atate wanga; ndi kwa mwala, Wandibala; pakuti anandipatsa Ine mbuyo, si nkhope yao; koma m'nthawi ya kubvutidwa kwao adzati, Ukani, tipulumutseni.

Yeremiya 2

Yeremiya 2:18-36