Yeremiya 2:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Monga mbala iri ndi manyazi pamene igwidwa, comweco nyumba ya Israyeli iri ndi manyazi; iwo, mafumu ao, akuru ao, ansembe ao, ndi aneneri ao;

Yeremiya 2

Yeremiya 2:20-27