Yeremiya 2:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma iri kuti milungu yako imene wadzipangira? Iuke, ikupulumutse iwe m'nthawi ya kubvutidwa kwako; pakuti milungu yako ilingana ndi kucuruka kwa midzi yako, Yuda iwe.

Yeremiya 2

Yeremiya 2:22-37