Numeri 23:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Balamu anati kwa Balaki, Ndimangireni kuno maguwa a nsembe asanu ndi awiri, nimundikonzere kuno ng'ombe zisanu ndi ziwiri, ndi nkhosa zamphongo zisanu ndi ziwiri.

2. Ndipo Balaki anacita monga Balamu ananena; ndipo Balaki ndi Balamu anapereka pa guwa la nsembe liri lonse ng'ombe ndi nkhosa yamphongo.

Numeri 23