Mateyu 25:44 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pomwepo iwonso adzayankha kuti, Ambuye, tinakuonani liti wanjala, kapena waludzu, kapena mlendo, kapena wamarisece, kapena m'nyumba yandende, ndipo ife sitinakutumikirani Inu?

Mateyu 25

Mateyu 25:39-46