Masalmo 43:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Tumizirani kuunika kwanu ndi coonadi canu zinditsogolere:Zindifikitse ku phiri lanu loyera,Kumene mukhala Inuko.

4. Kuti ndipite kufikira guwa la nsembe la Mulungu,Kufikira Mulungu wa cimwemwe canga ceniceni:Ndi kuti ndikuyamikeni ndi zeze, Mulungu, Mulungu wanga.

5. Udziweramiranji moyo wanga iwe?Ndi kuzingwa m'kati mwanga?Yembekeza Mulungu: pakuti ndidzamyamikanso,Ndiye cipulumutso ca nkhope yanga, ndi Mulungu wanga.

Masalmo 43