Marko 7:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Afarisi ndi alembi anamfunsa Iye, kuti, Bwanji ophunzira anu satsata mwambo wa akuru, koma akudya mkate wao ndi m'manja mwakuda?

Marko 7

Marko 7:1-12