Deuteronomo 3:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa ine, Usamuopa; popeza ndampereka iye ndi anthu ace onse, ndi dziko lace, m'dzanja lako; umcitire monga umo unacitira Sihoni mfumu ya Aamori, amene anakhala m'Hesiboni.

Deuteronomo 3

Deuteronomo 3:1-3