2 Mafumu 4:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Elisa anabwera ku Giligala, koma m'dzikomo munali njala; ndi ana a aneneri anali kukhala pansi pamaso pace; ndipo anati kwa mnyamata wace, Ika nkhali yaikuruyo, uphikire ana a aneneri.

2 Mafumu 4

2 Mafumu 4:31-42