1 Samueli 9:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene analikutsika polekeza mudzi, Samueli ananena ndi Sauli, Uzani mnyamatayo abatsogola; napita iyeyo. Koma inu muime pano, kuti ndikumvetseni mau a Mulungu.

1 Samueli 9

1 Samueli 9:18-27