1 Samueli 14:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Sauli analikukhala m'matsekerezo a Gibeya patsinde pa mtengo wankhangaza uli ku Migroni; ndipo panali naye anthu monga mazana asanu ndi limodzi;

1 Samueli 14

1 Samueli 14:1-7