1 Mbiri 17:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace tsono, uzitero naye mtumiki wanga Davide, Atero Ambuye wa makamu, Ndinakutenga kubusa potsata iwe nkhosa, kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga Israyeli;

1 Mbiri 17

1 Mbiri 17:1-14