1 Mbiri 17:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pali ponse ndinayenda nao Aisrayeli onse ndinanena kodi mau ndi woweruza ali yense wa Israyeli, amene ndinamuuza adyetse anthu anga, ndi kuti, Mwalekeranji kundimangira nyumba yamikungudza?

1 Mbiri 17

1 Mbiri 17:1-15