1 Mafumu 20:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mneneri uja anayandikira kwa mfumu ya Israyeli, nati kwa iye, Kadzilimbitseni, mudziwe mucenjere ndi cimene mucicita; popeza caka cikudzaci mfumu ya Aramu idzabweranso kulimbana nanu.

1 Mafumu 20

1 Mafumu 20:15-24