1 Atesalonika 3:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kuti akakhazikitse mitima yanu yopanda cifukwa m'ciyero pamaso pa Mulungu Atate wathu, pakufika Ambuye wathu Yesu pamodzi ndi oyera mtima ace onse.

1 Atesalonika 3

1 Atesalonika 3:7-13