Zefaniya 3:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Tsoka uyo wopanduka, ndi wodetsedwa, ndiye mudzi wozunza!

2. Sanamvera mau, sanalola kulangizidwa; sanakhulupirira Yehova, sanayandikira kwa Mulungu wace.

Zefaniya 3