Yoswa 3:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pakhale dera pakati pa inu ndi ilo, monga mikono zikwi ziwiri poliyesa; musaliyandikire, kuti mudziwe njira imene muziyendamo; popeza simunapita njirayi kufikira lero.

Yoswa 3

Yoswa 3:1-13