Yoswa 2:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anayenda iwo, nafika kuphiri, nakhalako masiku atatu mpaka atabwerera olondolawo; popeza olondolawo anawafunafuna panjira ponse, osawapeza.

Yoswa 2

Yoswa 2:20-24