Yoswa 12:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo awa ndi mafumu a dzikolo amene ana a Israyeli anwakantha, nalanda dziko lao tsidya la Yordano kum'mawa, kuyambira cigwa ca Arimoni, mpaka phiri la Herimoni, ndi cidikha conse ca kum'mawa;

Yoswa 12

Yoswa 12:1-2