Yohane 1:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yohane acita umboni za iye, napfuula nati, Uyu ndiye amene ndinanena za iye, Wakudzayo pambuyo panga analipo ndisanabadwe ine; cifukwa anakhala woyamba wa ine.

Yohane 1

Yohane 1:8-19