Yesaya 8:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene iwo adzati kwa iwe, Funa kwa olaula, ndi obwebweta, amene alira pyepye, nang'ung'udza; kodi anthu sadzafuna kwa Mulungu wao? Cifukwa ca amoyo, kodi adzafuna kwa akufa?

Yesaya 8

Yesaya 8:10-22