Yesaya 66:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti zonsezi mkono wanga wazilenga, momwemo zonsezi zinaoneka, ati Yehova; koma ndidzayang'anira munthu uyu amene ali waumphawi, ndi wa mzimu wosweka, nanthunthumira ndi mau anga.

Yesaya 66

Yesaya 66:1-3