Yesaya 66:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Yehova, Kumwamba ndi mpando wanga wacifumu, ndi dziko lapansi ndi coikapo mapazi anga; mudzandimangira Ine nyumba yotani? ndi malo ondiyenera kupumamo ali kuti?

Yesaya 66

Yesaya 66:1-7