Yesaya 64:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo palibe amene aitana dzina lanu, amene adzikangamiza yekha kugwiritsa Inu; pakuti Inu mwatibisira nkhope yanu, ndipo mwatinyeketsa ndi zoipa zathu.

Yesaya 64

Yesaya 64:6-12