Yesaya 64:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ife tonse takhala ngati wina amene ali wosakonzeka; ndi zolungama zathu zonse ziri ngati cobvala codetsedwa; ndipo ife tonse tifota monga tsamba, ndi zoipa zathu zitiuluza monga mphepo.

Yesaya 64

Yesaya 64:1-9