Yesaya 6:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamwamba pa Iye panaima aserafi; yense anali ndi mapiko asanu ndi limodzi; awiri anaphimba nao nkhope yace, awiri naphimba nao mapazi ace, awiri nauluka nao.

Yesaya 6

Yesaya 6:1-11