Yesaya 53:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iye adzaona zotsatira mabvuto a moyo wace, nadzakhuta nazo; ndi nzeru zace mtumiki wanga wolungama adzalungamitsa ambiri, nadzanyamula mphulupulu zao.

Yesaya 53

Yesaya 53:3-12