Yesaya 5:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa kuti munda wamphesa wa Yehova wa makamu ndiwo banja la Israyeli, ndi anthu a Yuda, mtengo wace womkondweretsa; Iye anayembekeza ciweruziro, koma onani kuphana; nayembekeza cilungamo, koma onani kupfuula.

Yesaya 5

Yesaya 5:1-15