Yesaya 48:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwe wacimva taona zonsezi; ndipo inu kodi inu simudzacinena? Ndakusonyeza iwe zinthu zatsopano kucokera nthawi yino, ngakhale zinthu zobisika, zimene iwe sunazidziwe.

Yesaya 48

Yesaya 48:3-16