Yesaya 45:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ine sindinanena m'tseri m'malo a dziko la mdima; Ine sindinati kwa mbeu ya Yakobo, Mundifune Ine mwacabe; Ine Yehova ndinena cilungamo, ndinena zimene ziri zoona.

Yesaya 45

Yesaya 45:9-25