Yesaya 43:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwe sunandigulire Ine nzimbe ndi ndarama, pena kundikhutitsa ndi mafuta a nsembe zako. Koma iwe wanditumikiritsa ndi macimo ako, wanditopetsa ndi mphulupulu zako.

Yesaya 43

Yesaya 43:20-25