Yesaya 39:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nthawi imeneyo Merodakibaladani, mwana wa Baladani, mfumu ya ku Babulo, anatumiza akalata ndi mphatso kwa Hezekiya; pakuti anamva kuti iye anadwala, nacira.

Yesaya 39

Yesaya 39:1-8