Yesaya 37:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace atero Yehova za mfumu ya Asuri, Iye sadzafika pa mudzi uno, ngakhale kuponyapo mubvi, ngakhale kufika patsogolo pace ndi cikopa, ngakhale kuunjikirapo mulu.

Yesaya 37

Yesaya 37:32-37