Yesaya 29:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo masomphenya onse akusandukirani mau a m'buku limatidwa ndi phula, limene anthu amapereka kwa wina wodziwa kuwerenga, nati, Werengani umu; koma ati, Sindingathe, cifukwa lamatidwa ndi phula;

Yesaya 29

Yesaya 29:9-12