Yesaya 28:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pangano lanu ndi imfa lidzathedwa, ndi kubvomerezana kwanu ndi kunsi kwa manda kudzalepereka; popita mliri woopsya udzakuponderezani pansi.

Yesaya 28

Yesaya 28:13-19