Yesaya 26:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi moyo wanga ndinakhumba Inu usiku; inde ndi mzimu wanga wa mwa ine ndidzafuna Inu mwakhama; pakuti pamene maweruziro anu ali pa dziko lapansi, okhala m'dziko lapansi adzaphunzira cilungamo.

Yesaya 26

Yesaya 26:1-19