Yesaya 26:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akufa anu adzakhala ndi moyo; mitembo yao idzauka. Ukani muyimbe, inu amene mukhala m'pfumbi; cifukwa mame ako akunga mame a pamasamba, ndipo dziko lapansi lidzaturutsa mizimu.

Yesaya 26

Yesaya 26:10-21