Yesaya 17:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsiku limenelo midzi yace yolimba idzakhala ngati mabwinja a m'nkhalango, ndi a pansonga pa phiri, osiyidwa pamaso pa ana a Israyeli; ndipo padzakhala bwinja.

Yesaya 17

Yesaya 17:2-14