Yeremiya 51:46 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mtima wanu usalefuke, musaope cifukwa ca mbiri imene idzamveka m'dzikomu; pakuti mbiri idzafika caka cina, pambuyo pace caka cina mbiri yina, ndi ciwawa m'dziko, wolamulira kumenyana ndi wolamulira.

Yeremiya 51

Yeremiya 51:39-56