Yeremiya 51:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo wandidya ine, wandiphwanya ine, wandiyesa ine ngati mbiya yopanda kanthu, wandimeza ngati ng'ona, wadzaza m'kamwa mwace ndi zotsekemera zanga, wanditaya ine,

Yeremiya 51

Yeremiya 51:33-44