Yeremiya 33:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Monga khamu la kuthambo silingathe kuwerengedwa, ndi mcenga wa kunyanja sungathe kuyesedwa; comweco ndidzacurukitsa mbeu za Davide mtumiki wanga, ndi Alevi akunditumikira Ine.

Yeremiya 33

Yeremiya 33:21-26