Yeremiya 14:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo udzati kwa iwo mau awa, Maso anga agwe misozi usana ndi usiku, asaleke; pakuti namwali mwana wa anthu anga wasweka ndi kusweka kwakukuru, ndi bala lopweteka kwambiri.

Yeremiya 14

Yeremiya 14:9-22