Yeremiya 11:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova anacha dzina lako, Mtengo waazitona wauwisi, wokoma wa zipatso zabwino; ndi mau a phokoso lalikuru wayatsa moto pamenepo, ndipo nthambi zace zatyoka.

Yeremiya 11

Yeremiya 11:11-17