Yakobo 1:9-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Koma mbale woluluka adzitamandire pa ukulu wace;

10. pakuti adzapita monga duwa la udzu,

11. Pakuti laturuka dzuwa ndi kutentha kwace, ndipo laumitsa udzu; ndipo lathothoka duwa lace, ndi ukoma wa maonekedwe ace waonongeka; koteronso wacuma adzafota m'mayendedwe ace.

12. Wodala munthu wakupirira poyesedwa; pakuti pamene wabvomerezeka, adzalandira korona wa moyo, amene Ambuye adalonjezera iwo akumkonda iye.

Yakobo 1