Yakobo 1:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti laturuka dzuwa ndi kutentha kwace, ndipo laumitsa udzu; ndipo lathothoka duwa lace, ndi ukoma wa maonekedwe ace waonongeka; koteronso wacuma adzafota m'mayendedwe ace.

Yakobo 1

Yakobo 1:6-15