Tito 3:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Okhulupirika mauwa, ndipo za izi ndifuna kuti ulimbitse mau, kuti iwo akukhulupirira Mulungu asamalire akhalebe atsogoleri a nchito zabwino. Izi nzokoma ndi zopindulitsa anthu;

9. koma pewa mafunso opusa, ndi mawerengedwe a mibadwo, ndi ndeu, ndi makani a pamalamulo; pakuti sizipindulitsa, ndipo ziri zacabe.

10. Munthu wopatukira cikhulupiriro, utamcenjeza kamodzi ndi kawiri, umkanize,

Tito 3