Oweruza 7:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi magulu atatuwo anaomba malipenga, naswa mbiyazo, nagwira miuni ndi dzanja lao lamanzere, ndi malipenga m'dzanja lao lamanja kuwaomba; ndipo anapfuula, Lupanga la Yehova ndi la Gideoni.

Oweruza 7

Oweruza 7:16-24